2 Samueli 9:6 BL92

6 Ndipo Mefiboseti mwana wa Jonatani, mwana wa Sauli, anafika kwa Davide, nagwa nkhope yace pansi, namlambira. Ndipo Davide anati, Mefiboseti! Nayankha iye, Ndine mnyamata wanu.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 9

Onani 2 Samueli 9:6 nkhani