10 Ndipo Yuda anamuka kwa Akanani akukhala m'Hebroni; koma kale dzina la Hebroni ndilo mudzi wa Ariba; ndipo anakantha Sesai, ndi Ahimani, ndi Talimai.
Werengani mutu wathunthu Oweruza 1
Onani Oweruza 1:10 nkhani