Oweruza 1:15 BL92

15 Ndipo anati kwa Iye, Mundipatse dalitso; popeza mwandipatsa dziko lakumwela, ndipatsenso zitsime za madzi. Pamenepo Kalebe anampatsa zitsime za kumtunda ndi zitsime za kunsi.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 1

Onani Oweruza 1:15 nkhani