Oweruza 11:2 BL92

2 Ndipo mkazi wa Gileadi anambalira ana amuna; koma atakula ana amuna a mkaziyo anampitikitsa Yefita, nanena naye, Sudzalandira colowa m'nyumba ya atate wako; pakuti ndiwe mwana wa mkazi wina.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 11

Onani Oweruza 11:2 nkhani