Oweruza 13:11 BL92

11 Nanyamuka Manowa natsata mkazi wace, namdzera mwamuna uja, nanena naye, Kodi ndinu mwamuna ujamunalankhulandimkaziyu? Ndipo anati, Ndine amene.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 13

Onani Oweruza 13:11 nkhani