Oweruza 20:21 BL92

21 Pamenepo ana a Benjamini anaturuka m'Gibeya, naononga a Israyeli tsiku lija zikwi makumi awiri mphambu ziwiri, kuwagoneka pansi,

Werengani mutu wathunthu Oweruza 20

Onani Oweruza 20:21 nkhani