Oweruza 20:23 BL92

23 Ndipo ana a Israyeli anakwera nalira misozi pamaso pa Yehova mpaka madzulo; nafunsira kwa Yehova ndi kuti, Ndiyandikizenso kodi kulimbana nkhondo ndi ana a Benjamini mbale wanga? Ndipo Yehova anati, Mumkwerere.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 20

Onani Oweruza 20:23 nkhani