Oweruza 20:25 BL92

25 Ndipo Benjamini anawaturukira ku Gibeya m'mawa mwace, naononganso a ana a Israyeli amuna zikwi khumi ndi zisanu ndi zitatu kuwagoneka pansi; ndiwo onse osolola lupanga.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 20

Onani Oweruza 20:25 nkhani