Oweruza 21:12 BL92

12 Ndipo anapeza mwa anthu a Yabesi-gileadi anamwali mazana anai osadziwa mwamuna mogona naye; nabwera nao kumisasa ku Silo, ndiwo a m'dziko la Kanani.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 21

Onani Oweruza 21:12 nkhani