Oweruza 21:5 BL92

5 Nati ana a Israyeli, Ndani iye mwa mapfuko onse a Israyeli amene sanakwera kudza kumsonkhano kwa Yehova? pakuti panali lumbiro lalikuru pa iye wosakwera kudza kwa Yehova ku Mizipa, ndi kuti, Aphedwe ndithu.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 21

Onani Oweruza 21:5 nkhani