12 Koma ana a Israyeli anaonjezanso kucita coipa pamaso pa Yehova; pamenepo Yehova analimbitsa Egiloni mfumu ya Moabu pa Israyeli, popeza anacita coipa pamaso pa Yehova.
Werengani mutu wathunthu Oweruza 3
Onani Oweruza 3:12 nkhani