Oweruza 3:9 BL92

9 Ndipo pamene ana a Israyeli anapfuula kwa Yehova, Yehova anaukitsira ana a Israyeli mpulumutsi amene anawapulumutsa, ndiye Otiniyeli mwana wa'Kenazi, mng'ono wace wa Kalebe.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 3

Onani Oweruza 3:9 nkhani