17 Koma Sisera anathawira coyenda pansi ku hema wa Yaeli mkazi wa Heberi Mkeni; pakuti panali mtendere pakati pa Yabini mfumu ya Hazori, ndi nyumba ya Heberi Mkeni.
Werengani mutu wathunthu Oweruza 4
Onani Oweruza 4:17 nkhani