Oweruza 6:28 BL92

28 Ndipo pakuuka mamawa amuna a ku mudziwo, taonani, guwa la nsembe la Baala litagamuka, ndi cifanizo cinali pomwepo citalikhidwa ndi ng'ombe yaciwiri yoperekedwa pa guwa la nsembe adalimanga.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 6

Onani Oweruza 6:28 nkhani