Oweruza 8:15 BL92

15 Ndipo anafika kwa amuna a ku Sukoti, nati, Tapenyani Zeba ndi Tsalimuna amene munanditonza nao ndi kuti, Kodi manja a Zeba ndi Tsalimuna akhala m'dzanja lako, kuti tiwaninkhe mkate amuna ako akulema?

Werengani mutu wathunthu Oweruza 8

Onani Oweruza 8:15 nkhani