Yohane 14:10 BL92

10 Sukhulupirira kodi kuti ndiri Ine mwa Atate, ndi Atate ali mwa Ine? Mau amene ndinena Ine kwa inu sindilankhula kwa Ine ndekha; koma Atate wokhala mwa Ine acita nchito zace.

Werengani mutu wathunthu Yohane 14

Onani Yohane 14:10 nkhani