Yohane 18:15 BL92

15 Koma Simoni Petro ndi wophunzira wina anatsata Yesu. Koma wophunzira ameneyo anali wodziwika kwa mkulu wa ansembe, nalowa pamodzi ndi Yesu, m'bwalo la mkulu wa ansembe;

Werengani mutu wathunthu Yohane 18

Onani Yohane 18:15 nkhani