Yohane 19:21 BL92

21 Pamenepo ansembe akulu a Ayuda, ananena kwa Pilato, Musalembe, Mfumu ya Ayuda; koma kuti Iyeyu anati, Ndiri Mfumu ya Ayuda.

Werengani mutu wathunthu Yohane 19

Onani Yohane 19:21 nkhani