Yohane 21:23 BL92

23 Cifukwa cace mau awa anaturuka kufikira kwa abale, kuti wophunzira uyu sadzafa. Koma Yesu sananena kwa iye kuti sadzafa; koma, Ngati ndifuna iye akhale kufikira ndidza, kuli ciani ndi iwe?

Werengani mutu wathunthu Yohane 21

Onani Yohane 21:23 nkhani