Yohane 21:6 BL92

6 Koma anati kwa iwo, Ponyani khoka ku mbali ya dzanja lamanja ya ngalawa, ndipo mudzapeza, Pamenepo anaponya, ndipo analibenso mphamvu yakulikoka cifukwa ca kucuruka nsomba.

Werengani mutu wathunthu Yohane 21

Onani Yohane 21:6 nkhani