Yohane 21:7 BL92

7 Pamenepo wophunzira uja amene Yesu anamkonda ananena kwa Petro, Ndiye Ambuye. Simoni Petro pakumva kuti ndiye Ambuye, anadzibveka maraya a pathupi, pakuti anali wamarisece, nadziponya yekha m'nyanja.

Werengani mutu wathunthu Yohane 21

Onani Yohane 21:7 nkhani