Yohane 5:19 BL92

19 Pamenepo Yesu anayankha nati kwa iwo, Indetu, indetu, ndinena kwa inu, sakhoza Mwana kucita kanthu pa yekha, koma cimene aona Atate acicita, ndico. Pakuti zimene iye azicita, zomwezo Mwananso azicita momwemo.

Werengani mutu wathunthu Yohane 5

Onani Yohane 5:19 nkhani