Yohane 8:42 BL92

42 Yesu anati kwa iwo, 4 Mulungu akadakhala Atate wanu, mukadakonda Ine; pakuti Ine ndinaturuka, ndi kucokera kwa Mulungu; pakuti sindinadza kwa Ine ndekha, koma Iyeyu anandituma Ine.

Werengani mutu wathunthu Yohane 8

Onani Yohane 8:42 nkhani