Yohane 9:16 BL92

16 Ena pamenepo mwa Afarisi ananena, Munthu uyu sacokera kwa Mulungu, cifukwa sasunga Sabata. Koma ena ananena, Munthu ali wocimwa, akhoza bwanji kucita zizindikilo zotere? Ndipo panali kutsutsana mwa iwo.

Werengani mutu wathunthu Yohane 9

Onani Yohane 9:16 nkhani