Yohane 9:17 BL92

17 Pamenepo ananenanso kwa wosaonayo, Iwe unenanji za iye, popeza anakutsegulira maso ako? Koma iye anati, Ali Mneneri.

Werengani mutu wathunthu Yohane 9

Onani Yohane 9:17 nkhani