22 monga iye anacitira ana a Bsau, akukhala m'Seiri, pamene anaononga Ahori pamaso pao; ndipo analanda dziko lao, nakhala m'malo mwao kufikira lero lomwe.
Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 2
Onani Deuteronomo 2:22 nkhani