Deuteronomo 23:14 BL92

14 popeza Yehova Mulungu wanu ayenda pakati pa cigono canu, kukupulumutsani ndi kupereka adani anu pamaso panu; cifukwa cace cigono canu cikhale copatulika; kuti angaone kanthu kodetsa mwa inu, ndi kukupotolokerani.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 23

Onani Deuteronomo 23:14 nkhani