Deuteronomo 23:18 BL92

18 Musamabwera nayo mphotho ya wacigololo, kapena mtengo wace wa garu kulowa nazo m'nyumba ya Yehova Mulungu wanu, cifukwa ca cowinda ciri conse; pakuti onse awiriwa Yehova Mulungu wanu anyansidwa nao.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 23

Onani Deuteronomo 23:18 nkhani