9 Yehova adzakukhazikirani yekha mtundu wa anthu wopatulika, monga anakulumbirirani; ngati mudzasunga malamulo a Yehova Mulungu wanu, ndi kuyenda m'njira zace.
Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28
Onani Deuteronomo 28:9 nkhani