Deuteronomo 31:10 BL92

10 Ndipo Mose anawauza, ndi kuti, Pakutha pace pa zaka zisanu ndi ziwiri, pa nyengo yoikika ya m'caka cakulekerera, pa madyerero a misasa;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 31

Onani Deuteronomo 31:10 nkhani