Deuteronomo 34:1 BL92

1 Ndipo Mose anakwera kucokera ku zidikha za Moabu, kumka ku phiri la Nebo, pamwamba pa Pisiga, popenyana ndi Yeriko. Ndipo Yehova anamuonetsa dziko lonse la Gileadi, kufikira ku Dani;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 34

Onani Deuteronomo 34:1 nkhani