Deuteronomo 34:9 BL92

9 Ndipo Yoswa mwana wa Nuni anadzala ndi mzimu wanzeru; popeza Mose adamuikira manja ace; ndi ana a Israyeli anamvera iye, nacita monga Yehova adauza Mose.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 34

Onani Deuteronomo 34:9 nkhani