Deuteronomo 5:16 BL92

16 Lemekeza atate wako ndi amako, monga Yehova Mulungu wako anakulamulira; kuti masiku ako acuruke, ndi kuti cikukomere, m'dziko limene Yehova Mulungu wako akupatsa iwe.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 5

Onani Deuteronomo 5:16 nkhani