Oweruza 1:17 BL92

17 Ndipo Yuda anamuka ndi Simeoni mkuru wace, nakantha Akanani akukhala m'Zefati, nauononga konse. Koma dzina la mudziwo analicha Horima.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 1

Onani Oweruza 1:17 nkhani