Oweruza 1:4 BL92

4 Ndipo Yuda atakwera, Yehova anapereka Akanani ndi Aperizi m'dzanja lao, ndipo anakantha a iwowa anthu zikwi khumi.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 1

Onani Oweruza 1:4 nkhani