Oweruza 11:21 BL92

21 Ndipo Yehova Mulungu wa Israyeli anapereka Sihoni ndi anthu ace onse m'dzanja la Israyeli, ndipo anawakantha, ndi Israyeli analandira colowa cace, dziko lonse la Aamori, nzika za m'dziko lija.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 11

Onani Oweruza 11:21 nkhani