Oweruza 11:20 BL92

20 Koma Sihoni sanakhulupirira Israyeli kuti apitire pakati pa malire ace; koma Sihoni anamemeza anthu ace onse, namanga misasa ku Yahazi, nathira nkhondo Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 11

Onani Oweruza 11:20 nkhani