Oweruza 11:27 BL92

27 Potero sindinakucimwirani ine, koma mundicitira coipa ndinu kundithira nkhondo; Yehova, Woweruzayo, aweruze lero lino pakati pa ana a Israyeli ndi ana a Amoni.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 11

Onani Oweruza 11:27 nkhani