14 Ndipo anali nao ana amuna makumi anai ndi zidzukulu zazimuna makumi atatu, akuyenda okwera pa ana a aburu makumi asanu ndi awiri; naweruza Israyeli zaka zisanu ndi zitatu.
Werengani mutu wathunthu Oweruza 12
Onani Oweruza 12:14 nkhani