Oweruza 12:3 BL92

3 Ndipo pakuona ine kuti simunandipulumutsa, ndinataya moyo wanga ndi kupita kwa ana a Amoni; ndipo Yehova anawapereka m'dzanja langa; mwakwereranji tsono lero lino kundicitira nkhondo?

Werengani mutu wathunthu Oweruza 12

Onani Oweruza 12:3 nkhani