Oweruza 13:8 BL92

8 Pamenepo Manowa anapembedza Yehova, nati, Yehova, ndikupemphani, atidzerenso munthu wa Mulungu mudamtumayo, natilangize ico tizicitira mwanayo akadzabadwa.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 13

Onani Oweruza 13:8 nkhani