4 Koma atate wace ndi amai wace sanadziwa kuti cidacokera kwa Yehova ici; popeza analikufuna kutola cifukwa ndi Afilisti. Ndipo nthawi ija Afilisti analamulira Israyeli.
Werengani mutu wathunthu Oweruza 14
Onani Oweruza 14:4 nkhani