Oweruza 16:21 BL92

21 Pamenepo Afilisti anamgwira, namkolowola maso, natsika naye ku Gaza, nammanga ndi maunyolo amkuwa; namperetsa m'kaidi.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 16

Onani Oweruza 16:21 nkhani