Oweruza 16:20 BL92

20 Ndipo anati, Afilisti akugwera, Samsoni. Nagalamuka iye m'tulo tace, nati, Ndizituruka ngati nthawi zina, ndi kudzitakasika. Koma sanadziwa kuti Yehova adamcokera.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 16

Onani Oweruza 16:20 nkhani