Oweruza 2:14 BL92

14 Pamenepo mkwiyo wa Yehova unayakira Israyeli, ndipo anawapereka m'manja a ofunkha kuti awafunkhe; nawagulitsa m'dzanja la adani ao akuwazungulira osakhozanso iwowo kuima pamaso pa adani ao.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 2

Onani Oweruza 2:14 nkhani