Oweruza 2:15 BL92

15 Kuli konse anaturuka, dzanja la Yehova linawakhalira moipa, monga Yehova adanena, ndi monga Yehova adawalumbirira; nasautsika kwambiri iwowa.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 2

Onani Oweruza 2:15 nkhani