Oweruza 5:4 BL92

4 Yehova, muja mudaturuka m'Seiri,Muja mudayenda kucokera ku thengo la Edomu,Dziko linanjenjemera, thambo lomwe linakha,Inde mitambo inakha madzi.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 5

Onani Oweruza 5:4 nkhani