Oweruza 6:18 BL92

18 Musacoke pano, ndikupemphani, mpaka ndikudzerani ndi kuturutsa copereka canga ndi kuciika pamaso panu. Ndipo anati, Ndidzalinda mpaka ubwera.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 6

Onani Oweruza 6:18 nkhani