Oweruza 7:14 BL92

14 Ndipo mnzace anayankha nati, Ici si cina konse koma lupanga la Gideoni mwana wa Yoasi, munthu wa Israyeli; Mulungu wapereka Midyani ndi a m'misasa onse m'dzanja lace.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 7

Onani Oweruza 7:14 nkhani