Oweruza 7:19 BL92

19 Motero Gideoni ndi amuna zana anali naye anafikira ku cilekezero ca misasa poyambira ulonda wa pakati, atasintha alonda tsopano apa; ndipo anaomba malipenga, naphwanya mbiya zokhala m'manja mwao.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 7

Onani Oweruza 7:19 nkhani